We’ve updated our Terms of Use to reflect our new entity name and address. You can review the changes here.
We’ve updated our Terms of Use. You can review the changes here.

Kodi Khristu anakhala bwanji munthu, popeza iye ndi Mulungu mwana?

from Mafunso Ndi Mayankho Vol. 3: Khristu Ndi Ntchito Zake (Chichewa) by Dana Dirksen

/

lyrics

5. Kodi Khristu anakhala bwanji munthu, popeza iye ndi Mulungu mwana?

Maria usaope
Wapeza chisomo ndi Mulungu
Udzakhala ndi pakati nudzabala mwana wa mmuna
Udzamutcha dzina lake Yesu (*2)

Adzakhala wamkulu
Adzatchulidwa mwana wa wamkulu (*2)
Adzakhala wamkulu
Adzatchulidwa mwana wamkulu (*2)

Ambuye adzampatsa ufumu wa Davite
Adzalamulira nyumba ya Yakobo
Ufumu wake sudzatha
Ufumu wake sudzatha
Maria usaope wapeza chisomo ndi Mulungu

Kodi Khristu anakhala bwanji Munthu?
Iye ponga Mulungu anakhala munthu pobadwa
Ndi mphamvu ya mzimu woyera ndi thupi ndi moyo
Mu mmimba mwanamwali Maria
Luka 1:20 mpaka 33
Maria

credits

license

all rights reserved

tags

about

Songs for Saplings Portland, Oregon

We create lively, fun songs that attempt to deliver the deepest Biblical truths in a format that children will love.

Songs for Saplings is James and Dana Dirksen. We live in Portland, OR, and have 6 beautiful children. We thank God that He has allowed us to share the Good News that Jesus came to seek and save that which was lost.

You can learn more about us at songsforsaplings.com
... more

contact / help

Contact Songs for Saplings

Streaming and
Download help

Redeem code

Report this track or account

If you like Songs for Saplings, you may also like: