We’ve updated our Terms of Use to reflect our new entity name and address. You can review the changes here.
We’ve updated our Terms of Use. You can review the changes here.

Kodi ungalape ndi kukhulupilira Khristu ndi mphamvu zako?

from Mafunso Ndi Mayankho Vol. 3: Khristu Ndi Ntchito Zake (Chichewa) by Dana Dirksen

/

lyrics

12. Kodi ungalape ndi kukhulupilira Khristu ndi mphamvu zako?

Ungalape?
Ungakhulupilire?
Ungalape ndukhulupilira Khristu ndi mphamvu zako? (*2)
Maso sanawone, makutu sanamve
Palibe amadziwa zomwe Mulungu wakonza kwa iwo womkonda
Mulungu wazionetsa kwa ine
Ndi mzimu wake wazionetsa kwa ine
Ndingalape
Ndingakhulupilire
Ndingalape ndikukhulupilira Khristu ndi Mphamvu yako

Sitinalandire mzimu wamdziko koma mzimu wa kwa Mulungu
Kuti tikamvetse zomwe Mulungu watipatsa ulere
Wandipatsa ulere
1 Akolinto 2
Wandipatsa ulere
Ungalape?
Ungakhulupilire

credits

license

all rights reserved

tags

about

Songs for Saplings Portland, Oregon

We create lively, fun songs that attempt to deliver the deepest Biblical truths in a format that children will love.

Songs for Saplings is James and Dana Dirksen. We live in Portland, OR, and have 6 beautiful children. We thank God that He has allowed us to share the Good News that Jesus came to seek and save that which was lost.

You can learn more about us at songsforsaplings.com
... more

contact / help

Contact Songs for Saplings

Streaming and
Download help

Redeem code

Report this track or account

If you like Songs for Saplings, you may also like: