We’ve updated our Terms of Use to reflect our new entity name and address. You can review the changes here.
We’ve updated our Terms of Use. You can review the changes here.

MPULUMUTSI WA OSANKHIDWA A MULUNGU NDI NDANI?

from Mafunso ndi Mayankho Vol. 2: KUGWA NDI CHIPULUMUTSO (Chichewa) by Dana Dirksen

/

lyrics

17. MPULUMUTSI WA OSANKHIDWA A MULUNGU NDI NDANI?

Ndani ndani ndani mpulumutsi
Mpulumutsi wa osankhidwa a Mulungu
Ndani ndani ndani mpulumutsi
Mpulumutsi waosankhidwa a Mulungu

Yekhayo mpulumutsi ndiye Yesu Khristu
Mwana wa muyaya wa Mulungu
Anakhala munthu, komanso ali Mlungu
Munthu m’modzi zilengedwe ziwiri

Ndine njira, choonadi ndi moyo
Palibe adza kwa Atate osadzera mwa Ine
Ine ndi njira, choonadi ndi moyo
Yohane 14 ndime 6
 

credits

license

all rights reserved

tags

about

Songs for Saplings Portland, Oregon

We create lively, fun songs that attempt to deliver the deepest Biblical truths in a format that children will love.

Songs for Saplings is James and Dana Dirksen. We live in Portland, OR, and have 6 beautiful children. We thank God that He has allowed us to share the Good News that Jesus came to seek and save that which was lost.

You can learn more about us at songsforsaplings.com
... more

contact / help

Contact Songs for Saplings

Streaming and
Download help

Redeem code

Report this track or account

If you like Songs for Saplings, you may also like: