We’ve updated our Terms of Use to reflect our new entity name and address. You can review the changes here.
We’ve updated our Terms of Use. You can review the changes here.

Usakhale nayo Milungu ina koma ine ndekha

from Mafunso Ndi Mayankho Vol. 4: Mau A Mulungu (Chichewa) by Dana Dirksen

/

lyrics

1. Usakhale nayo Milungu ina koma ine ndekha

Tsono Mose anatsika kuphiri
Kupita kwa anthu
Anachoka kuphiri anati Mulungu wanena izi kwa inu (*2)

Ndinakuchotsani m’dziko la iguputo dziko la ukapolo
Musakhale ndi milungu ina koma ine
Musakhale ndi milungu ina, ine ndekha

Tsono Mose anatsika kuphiri
Kupita kwa anthu
Anachoka kuphiri anati Mulungu wanena izi kwa inu

Mulungu wanena izi kwa inu
Mose anatsika, kutsika kuphiri
Ekisodo 20
Anatsika kuphiri anati
Mulungu wanena izi kwa inu

credits

license

all rights reserved

tags

about

Songs for Saplings Portland, Oregon

We create lively, fun songs that attempt to deliver the deepest Biblical truths in a format that children will love.

Songs for Saplings is James and Dana Dirksen. We live in Portland, OR, and have 6 beautiful children. We thank God that He has allowed us to share the Good News that Jesus came to seek and save that which was lost.

You can learn more about us at songsforsaplings.com
... more

contact / help

Contact Songs for Saplings

Streaming and
Download help

Redeem code

Report this track or account

If you like Songs for Saplings, you may also like: